Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 14:5 - Buku Lopatulika

Tomasi ananena ndi Iye, Ambuye, sitidziwa kumene munkako; tidziwa njira bwanji?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Tomasi ananena ndi Iye, Ambuye, sitidziwa kumene munkako; tidziwa njira bwanji?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tomasi adati, “Ambuye, sitikudziŵa kumene mukupita, nanga njira yake tingaidziŵe bwanji?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tomasi anati kwa Iye, “Ambuye ife sitikudziwa kumene Inu mukupita, nanga tingadziwe bwanji njirayo?”

Onani mutuwo



Yohane 14:5
10 Mawu Ofanana  

Filipo, ndi Bartolomeo; Tomasi, ndi Mateyu wamsonkho yo; Yakobo mwana wa Alifeyo, ndi Tadeyo;


Ndipo Iye anawayankha nanena, Mbadwo wosakhulupirira inu, ndidzakhala ndi inu kufikira liti? Ndidzakulekererani nthawi yanji? Mudze naye kwa Ine.


Ndipo Iye anati kwa iwo, Opusa inu, ndi ozengereza mtima kusakhulupirira zonse adazilankhula aneneri!


Pamenepo Tomasi, wotchedwa Didimo, anati kwa ophunzira anzake, Tipite ifenso kuti tikafere naye pamodzi.


Ndipo kumene ndinkako Ine, mudziwa njira yake.


Lamulo langa ndi ili, kuti mukondane wina ndi mnzake, monga ndakonda inu.


Koma tsopano ndimuka kwa Iye wondituma Ine; ndipo palibe wina mwa inu andifunsa Ine, Munka kuti?