Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 13:30 - Buku Lopatulika

Pamenepo iyeyo m'mene adalandira nthongo, anatuluka pomwepo. Koma kunali usiku.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamenepo iyeyo m'mene adalandira nthongo, anatuluka pomwepo. Koma kunali usiku.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yudasi atalandira mkate uja, pompo adatuluka. Nthaŵiyo nkuti kutada kale.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Nthawi yomweyo Yudasi atangodya buledi, anatuluka, ndipo unali usiku.

Onani mutuwo



Yohane 13:30
6 Mawu Ofanana  

Pakuti akapanda kuchita zoipa, samagona; ndipo akapanda kukhumudwitsa wina, tulo tao tiwachokera.


Mapazi ao athamangira koipa, ndipo iwo afulumira kukhetsa mwazi wosachimwa; maganizo ao ali maganizo oipa; bwinja ndi chipasuko zili m'njira mwao.


Masiku onse, pamene ndinali ndi inu mu Kachisi, simunatanse manja anu kundigwira: koma nyengo ino ndi yanu, ndipo ulamuliro wa mdima ndi wanu.


Ndipo Yesu anayankha, Ndi iyeyu, amene Ine ndidzamsunsira nthongo ndi kumpatsa. Pamenepo, m'mene anasunsa nthongo anaitenga naipatsa Yudasi mwana wa Simoni Iskariote.


miyendo yao ichita liwiro kukhetsa mwazi;