Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 13:25 - Buku Lopatulika

Iyeyu potsamira pomwepo, pa chifukwa cha Yesu, anena ndi Iye, Ambuye, ndiye yani?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Iyeyu potsamira pomwepo, pa chifukwa cha Yesu, anena ndi Iye, Ambuye, ndiye yani?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamenepo iyeyo adatsamira pachifukwa pa Yesu, namufunsa kuti, “Ambuye, mukunena yani kodi?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atamutsamiranso Yesuyo, anamufunsa Iye kuti, “Ambuye, kodi ndani?”

Onani mutuwo



Yohane 13:25
4 Mawu Ofanana  

Pamenepo mfumu Ahasuwero inalankhula, niti kwa mkazi wamkulu Estere, Ndani uyu, ali kuti iyeyu wadzazidwa mtima wake kuti azitero?


Pamenepo Simoni Petro anamkodola nanena naye, Utiuze ndiye yani amene anena za iye.


Petro, m'mene anacheuka, anapenya wophunzira amene Yesu anamkonda alikutsata, amenenso anatsamira pachifuwa pake pamgonero, nati, Ambuye, ndani iye wakupereka Inu?