Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 13:22 - Buku Lopatulika

Ophunzira analikupenyana wina kwa mnzake, ndi kusinkhasinkha kuti ananena za yani.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ophunzira analikupenyana wina kwa mnzake, ndi kusinkhasinkha kuti ananena za yani.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ophunzira aja adayamba kupenyetsetsana, osadziŵa konse kuti akunena yani.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ophunzira ake anapenyetsetsana wina ndi mnzake, posadziwa kuti amanena za yani.

Onani mutuwo



Yohane 13:22
9 Mawu Ofanana  

Ndipo anaona Yakobo kuti mu Ejipito munali tirigu, nati Yakobo kwa ana ake aamuna, Chifukwa chanji mulinkuyang'anana?


ndipo m'mene analinkudya, Iye anati, Indetu ndinena kwa inu, mmodzi wa inu adzandipereka Ine.


Ndipo iwo anagwidwa ndi chisoni chachikulu, nayamba kunena kwa Iye mmodzimmodzi, Kodi ndine, Ambuye?


Ndipo pamene anaseama iwo kudya, Yesu anati, Ndithu ndinena ndi inu, Mmodzi wa inu adzandipereka Ine, ndiye wakudya ndi Ine pamodzi.


Anayamba iwo kukhala ndi chisoni, ndi kunena naye mmodzimmodzi, kuti, Ndine kodi?


Koma onani, dzanja lake la iye amene adzandipereka ali pagome pano pamodzi ndi Ine.


Ndipo anayamba kufunsana mwa iwo okha, ndiye yani mwa iwo amene adzachita ichi.


Sindinena za inu nonse; ndidziwa amene ndawasankha: koma kuti cholemba chikwaniridwe, Iye wakudya mkate wanga anatsalimira pa Ine chidendene chake.


Yesu m'mene adanena izi, anavutika mumzimu, nachita umboni, nati, Indetu, indetu, ndinena ndi inu, kuti mmodzi wa inu adzandipereka Ine.