Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 11:6 - Buku Lopatulika

Chifukwa chake pamene anamva kuti anadwala, anakhala pamenepo pamalo pomwepo masiku awiri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chifukwa chake pamene anamva kuti anadwala, anakhala pamenepo pa malo pomwepo masiku awiri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Komabe pamene adamva za matendawo, Yesu adaswera masiku aŵiri pamalo pomwe adaaliripo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma atamva kuti Lazaro akudwala, Iye anakhalabe kumene anali masiku ena awiri.

Onani mutuwo



Yohane 11:6
10 Mawu Ofanana  

Ndipo Abrahamu anatcha dzina lake la malowo Yehova-Yire: monga ati lero lomwe, M'phiri la Yehova chidzaoneka.


Ndipo anawafotokozera iwo nalira, nawatembenukiranso, nanena nao, nampatula Simeoni mwa iwo, nammanga iye pamaso pao.


Chifukwa chake Yehova adzadikira, kuti akukomereni mtima, ndipo chifukwa chake Iye adzakuzidwa, kuti akuchitireni inu chifundo; pakuti Yehova ndiye Mulungu wa chiweruziro; odala ali onse amene amdikira Iye.


Koma Yesu anakonda Marita, ndi mbale wake, ndi Lazaro.


Ndipo pambuyo pake ananena kwa ophunzira ake, Tiyeni tipitenso ku Yudeya.