Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 11:30 - Buku Lopatulika

(Koma Yesu sanafike kumudzi, koma anali pamalo pomwe Marita adakomana ndi Iye.)

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

(Koma Yesu sanafike kumudzi, koma anali pamalo pomwe Marita adakomana ndi Iye.)

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamenepo nkuti Yesu asanafike kumudziko, koma anali chikhalire pamalo pomwe Marita adaakumana naye.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsopano nʼkuti Yesu asanalowe mʼmudzi, koma anali akanali pa malo pamene Marita anakumana naye.

Onani mutuwo



Yohane 11:30
3 Mawu Ofanana  

Pamenepo Marita, pakumva kuti Yesu alinkudza, anamuka kukakomana ndi Iye; koma Maria anakhalabe m'nyumba.


Ndipo m'mene anati ichi anachoka naitana Maria mbale wake m'tseri, ndi kuti, Wafika Mphunzitsi, akuitana iwe.


Koma iyeyo, pakumva, ananyamuka msanga, nadza kwa Iye.