Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 11:23 - Buku Lopatulika

Yesu ananena naye, Mlongo wako adzauka.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Yesu ananena naye, Mlongo wako adzauka.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu adamuuza kuti, “Mlongo wako adzauka.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yesu anati kwa iye, “Mlongo wako adzauka.”

Onani mutuwo



Yohane 11:23
4 Mawu Ofanana  

Koma ngakhale tsopano ndidziwa kuti zinthu zilizonse mukapempha Mulungu, adzakupatsani Mulungu.


Marita ananena ndi Iye, Ndidziwa kuti adzauka m'kuuka tsiku lomaliza.


Yesu ananena naye, Kodi sindinati kwa iwe, kuti, ngati ukhulupirira, udzaona ulemerero wa Mulungu?