Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 11:14 - Buku Lopatulika

Pamenepo Yesu anati kwa iwo momveka, Lazaro wamwalira.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamenepo Yesu anati kwa iwo momveka, Lazaro wamwalira.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Yesu adaŵauza mosabisa kuti, “Lazaro wamwalira,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo kenaka anawawuza momveka kuti, “Lazaro wamwalira.

Onani mutuwo



Yohane 11:14
6 Mawu Ofanana  

Ndipo mauwo ananena poyera. Ndipo Petro anamtenga Iye, nayamba kumdzudzula.


Pamenepo Ayuda anamzungulira Iye, nanena ndi Iye, Kufikira liti musinkhitsasinkhitsa moyo wathu? Ngati Inu ndinu Khristu, tiuzeni momveka.


Koma Yesu adanena za imfa yake; koma iwowa anayesa kuti ananena za mpumulo wa tulo.


Ndipo ndikondwera chifukwa cha inu kuti kunalibe Ine komweko, chakuti mukakhulupirire; koma tiyeni, tipite kwa iye.


Zinthu izi ndalankhula ndi inu m'mafanizo; ikudza nthawi imene sindidzalankhula ndi inu m'mafanizo, koma ndidzakulalikirani inu m'mafanizo, koma ndidzakulalikirani inu momveka za Atate.


Ophunzira ake ananena, Onani, tsopano mulankhula zomveka, ndipo mulibe kunena chiphiphiritso.