Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 11:12 - Buku Lopatulika

Chifukwa chake ophunzira ake anati kwa Iye, Ambuye, ngati ali m'tulo adzachira.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chifukwa chake ophunzira ake anati kwa Iye, Ambuye, ngati ali m'tulo adzachira.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo ophunzira ake adati, “Ambuye, ngati wagona tulo, achira.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ophunzira ake anayankha kuti, “Ambuye, ngati wagona adzapeza bwino.”

Onani mutuwo



Yohane 11:12
3 Mawu Ofanana  

ananena, Tulukani, pakuti kabuthuko sikanafe koma kali m'tulo. Ndipo anamseka Iye pwepwete.


Izi anati, ndipo zitatha izi ananena nao, Lazaro bwenzi lathu ali m'tulo; koma ndimuka kukamuukitsa iye tulo take.


Koma Yesu adanena za imfa yake; koma iwowa anayesa kuti ananena za mpumulo wa tulo.