Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 10:42 - Buku Lopatulika

Ndipo ambiri anakhulupirira Iye komweko.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ambiri anakhulupirira Iye komweko.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Motero anthu ambiri adakhulupirira Yesu kumeneko.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo pamalo amenewo ambiri anakhulupirira Yesu.

Onani mutuwo



Yohane 10:42
7 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake ambiri a mwa Ayuda amene anadza kwa Maria, m'mene anaona chimene anachita, anakhulupirira Iye.


Kungakhale kotero, ambiri a mwa akulu anakhulupirira Iye; koma chifukwa cha Afarisi sanavomereze, kuti angaletsedwe m'sunagoge,


Koma pamene anali mu Yerusalemu pa Paska pachikondwerero, ambiri anakhulupirira dzina lake, pakuona zizindikiro zake zimene anachitazi.


Ndipo m'mzinda muja anthu Asamariya ambiri anamkhulupirira Iye chifukwa cha mau a mkazi, wochita umboniyo, kuti, Anandiuza ine zinthu zilizonse ndinazichita.


Ndipo ambiri oposa anakhulupirira chifukwa cha mau ake;


Koma ambiri a m'khamu la anthu anakhulupirira Iye; ndipo ananena, Pamene Khristu akadza kodi adzachita zizindikiro zambiri zoposa zimene adazichita ameneyo?


Pakulankhula Iye zimenezi ambiri anakhulupirira Iye.