Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 10:23 - Buku Lopatulika

Ndipo Yesu analikuyendayenda mu Kachisi m'khonde la Solomoni.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yesu analikuyendayenda m'Kachisi m'khonde la Solomoni.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu ankangodziyendera m'Nyumba ya Mulungu, m'khonde lotchedwa Khonde la Solomoni.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ndipo Yesu ankayenda mʼbwalo la Nyumbayo ku malo a Solomoni.

Onani mutuwo



Yohane 10:23
3 Mawu Ofanana  

Koma kunali phwando la kukonzetsanso mu Yerusalemu; nyengoyo ndi yachisanu.


Koma m'mene anagwira Petro ndi Yohane, anawathamangira pamodzi anthu onse kukhonde lotchedwa la Solomoni, alikudabwa ndithu.


Ndipo mwa manja a atumwi zizindikiro ndi zozizwa zambiri zinachitidwa pa anthu; ndipo anali onse ndi mtima umodzi m'khonde la Solomoni.