Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 10:19 - Buku Lopatulika

Panakhalanso kutsutsana pakati pa Ayuda chifukwa cha mau awa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Panakhalanso kutsutsana pakati pa Ayuda chifukwa cha mau awa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Anthu adaayambanso kutsutsana okhaokha chifukwa cha mau ameneŵa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pa mawu awa Ayuda anagawikananso.

Onani mutuwo



Yohane 10:19
9 Mawu Ofanana  

Pamenepo Ayuda anatetana wina ndi mnzake ndi kunena, Akhoza bwanji ameneyu kutipatsa ife kudya thupi lake?


Ena pamenepo mwa Afarisi ananena, Munthu uyu sachokera kwa Mulungu, chifukwa sasunga Sabata. Koma ena ananena, Munthu ali wochimwa akhoza bwanji kuchita zizindikiro zotere? Ndipo panali kutsutsana mwa iwo.


Ndipo khamu la mzindawo linagawikana; ena anali ndi Ayuda, koma ena anali ndi atumwi.


Pakutitu poyamba posonkhana inu mu Mpingo, ndimva kuti pakhala malekano mwa inu; ndipo ndivomereza penapo.


pakuti, pokhala pali nkhwidzi ndi ndeu pakati pa inu simuli athupi kodi, ndi kuyendayenda monga mwa munthu?