Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 10:13 - Buku Lopatulika

chifukwa ali wolipidwa, ndipo sasamala nkhosa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

chifukwa ali wolipidwa, ndipo sasamala nkhosa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Wolembedwa ntchito uja amathaŵa, chifukwa amangotsata malipiro chabe, ndipo salabadirako za nkhosazo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Munthuyo amathawa chifukwa ndi wantchito ndipo sasamalira chilichonse cha nkhosazo.

Onani mutuwo



Yohane 10:13
7 Mawu Ofanana  

Wolipidwa amene sakhala mbusa, amene nkhosa sizili zake za yekha, aona mmbulu ulinkudza, nasiya nkhosazo, nathawa; ndipo mmbulu uzikwatula, nuzibalalitsa;


Ine ndiye Mbusa Wabwino; ndipo ndizindikira zanga, ndi zanga zindizindikira Ine,


Koma ananena ichi si chifukwa analikusamalira osauka, koma chifukwa anali mbala, ndipo pokhala nalo thumba, amaba zoikidwamo.


Ndipo anamgwira Sostene, mkulu wa sunagoge, nampanda kumpando wachiweruziro. Ndipo Galio sanasamalire zimenezi.


Koma ndifuna kuti mukhale osalabadira. Iye amene wosakwatira alabadira zinthu za Ambuye, kuti akondweretse Ambuye;


koma iye wokwatira alabadira zinthu za dziko lapansi, kuti akondweretse mkazi wake.


Pakuti ndilibe wina wa mtima womwewo, amene adzasamalira za kwa inu ndi mtima woona.