Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 1:36 - Buku Lopatulika

ndipo poyang'ana Yesu alikuyenda, anati, Onani Mwanawankhosa wa Mulungu!

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo poyang'ana Yesu alikuyenda, anati, Onani Mwanawankhosa wa Mulungu!

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene adaona Yesu akuyenda, iye adati, “Suuyu Mwanawankhosa wa Mulungu.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye ataona Yesu akudutsa anati, “Taonani Mwana Wankhosa wa Mulungu!”

Onani mutuwo



Yohane 1:36
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Isaki ananena ndi Abrahamu atate wake, nati, Atate wanga; ndipo iye anati, Ndine pano, mwana wanga. Ndipo anati, Taonani moto ndi nkhuni; koma mwanawankhosa wa nsembe yopsereza ali kuti?


Yang'anani kwa Ine, mupulumutsidwe, inu malekezero onse a dziko; pakuti Ine ndine Mulungu, palibe wina.


M'mawa mwake anaona Yesu alinkudza kwa iye, nanena, Onani Mwanawankhosa wa Mulungu amene achotsa tchimo lake la dziko lapansi!


Ndipo ophunzira awiriwo anamva iye alinkulankhula, natsata Yesu.


Yesu, ameneyo, chifukwa cha chimwemwe choikidwacho pamaso pake, anapirira mtanda, nanyoza manyazi, nakhala padzanja lamanja la mpando wachifumu wa Mulungu.