Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 1:35 - Buku Lopatulika

M'mawa mwakenso analikuimirira Yohane ndi awiri a ophunzira ake;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

M'mawa mwakenso analikuimirira Yohane ndi awiri a ophunzira ake;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

M'maŵa mwakenso Yohane anali pamalo pomwepo pamodzi ndi ophunzira ake ena aŵiri.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pa tsiku lotsatira Yohane analinso pamenepo pamodzi ndi awiri a ophunzira ake.

Onani mutuwo



Yohane 1:35
5 Mawu Ofanana  

Pamenepo iwo akuopa Yehova analankhulana wina ndi mnzake; ndipo Yehova anawatchera khutu namva, ndi buku la chikumbutso linalembedwa pamaso pake, la kwa iwo akuopa Yehova, nakumbukira dzina lake.


M'mawa mwake anaona Yesu alinkudza kwa iye, nanena, Onani Mwanawankhosa wa Mulungu amene achotsa tchimo lake la dziko lapansi!


M'mawa mwake anafuna kutuluka kunka ku Galileya, napeza Filipo. Ndipo Yesu ananena naye, Tsata Ine.


Ndipo tsiku lachitatu panali ukwati mu Kana wa mu Galileya; ndipo amake wa Yesu anali komweko.