Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 1:24 - Buku Lopatulika

Ndipo otumidwawo anali a kwa Afarisi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo otumidwawo anali a kwa Afarisi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Anthu aja adaaŵatuma ndi Afarisi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsopano Afarisi ena amene anatumidwa

Onani mutuwo



Yohane 1:24
13 Mawu Ofanana  

Mfarisi iwe wakhungu, yambawatsuka m'kati mwa chikho ndi mbale, kuti kunja kwake kukhalenso koyera.


Ndipo pamene Iye anatuluka m'menemo, alembi ndi Afarisi anayamba kumuumiriza Iye kolimba, ndi kumfunsa zinthu zambiri;


Koma Afarisi, ndiwo okonda ndalama, anamva izi zonse; ndipo anamseka.


Koma Afarisi ndi achilamulo anakaniza uphungu wa Mulungu kwa iwo okha, popeza sanabatizidwe ndi iye.


Anati, Ndine mau a wofuula m'chipululu, Lungamitsani njira ya Mbuye, monga anati Yesaya mneneriyo.


Ndipo anamfunsa iye, nati kwa iye, Koma ubatiza bwanji, ngati suli Khristu, kapena Eliya, kapena Mneneriyo?


Pakutitu Asaduki anena kuti kulibe kuuka kwa akufa, kapena mngelo, kapena mzimu; koma Afarisi avomereza ponse pawiri.


andidziwa ine chiyambire, ngati afuna kuchitapo umboni, kuti ndinakhala Mfarisi monga mwa mpatuko wolunjikitsitsa wa chipembedzero chathu.