Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 1:20 - Buku Lopatulika

Ndipo anavomera, wosakana; nalola kuti, Sindine Khristu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anavomera, wosakana; nalola kuti, Sindine Khristu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Iye adayankha mosabisa konse, adanenetsa ndithu kuti, “Inetu sindine Mpulumutsi wolonjezedwa uja ai.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye sanalephere kuvomereza, koma iye anavomereza momasuka kuti, “Ine sindine Khristu.”

Onani mutuwo



Yohane 1:20
6 Mawu Ofanana  

Iye sindiye kuunikaku, koma anatumidwa kukachita umboni wa kuunikaku.


Ndipo pakukwaniritsa njira yake Yohane, ananena, Muyesa kuti ine ndine yani? Ine sindine Iye. Koma taonani, akudza wina wonditsata ine, amene sindiyenera kummasulira nsapato za pa mapazi ake.