Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yeremiya 7:1 - Buku Lopatulika

Mau amene anadza kwa Yeremiya kuchokera kwa Yehova, kuti,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mau amene anadza kwa Yeremiya kuchokera kwa Yehova, kuti,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chauta adauza Yeremiya mau aŵa akuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mawu amene Yehova anayankhula kwa Yeremiya ndi awa,

Onani mutuwo



Yeremiya 7:1
5 Mawu Ofanana  

Ndipo mau a Yehova anadza kwa iye, nati,


Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, nati,


Mau amene anadza kwa Yeremiya za anthu onse a Yuda chaka chachinai cha Yehoyakimu mwana wake wa Yosiya, mfumu ya Yuda; ndicho chaka choyamba cha Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni;


Anthu adzawatcha nthale ya siliva, pakuti Yehova wakana iwo.


Ima m'chipata cha nyumba ya Yehova, lalikira m'menemo mau awa, ndi kuti, Tamvani mau a Yehova, inu nonse a Yuda, amene alowa m'zipata izi kuti mugwadire Yehova.