Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yeremiya 51:4 - Buku Lopatulika

Ndipo adzagwa ophedwa m'dziko la Ababiloni, opyozedwa m'miseu yake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo adzagwa ophedwa m'dziko la Ababiloni, opyozedwa m'miseu yake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adzavulazidwa ndi kufera m'dziko lonse ndi m'miseu ya mzinda wao womwe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Adzavulazidwa ndi kufera mʼdziko la Babuloni lomwelo ndi mʼmisewu yawo yomwe.

Onani mutuwo



Yeremiya 51:4
6 Mawu Ofanana  

Onse opezedwa adzapyozedwa, ndi onse ogwidwa adzagwa ndi lupanga.


Koma iwe watayidwa kunja kwa manda ako, ngati nthambi yonyansa, ngati chovala cha ophedwa, opyozedwa ndi lupanga, otsikira kumiyala ya dzenje, monga ngati mtembo wopondedwa ndi phazi.


Chifukwa chake anyamata ake adzagwa m'miseu yake, ndipo anthu onse a nkhondo adzatontholetsedwa tsiku lomwelo, ati Yehova wa makamu.


Chifukwa chake anyamata ake adzagwa m'miseu yake, ndi anthu ankhondo ake onse adzatontholetsedwa tsiku lomwelo, ati Yehova.


Lupanga lili pa akavalo ao, ndi pa magaleta ao, ndi pa anthu onse osakanizidwa amene ali pakati pake, ndipo adzakhala ngati akazi; lupanga lili pa chuma chake, ndipo chidzalandidwa.


Ngakhale Babiloni adzakwera kumwamba, ngakhale adzalimbitsa msanje wa mphamvu yake, koma kuchokera kwa Ine akufunkha adzafika kwa iye, ati Yehova.