Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yeremiya 48:4 - Buku Lopatulika

Mowabu waonongedwa; ang'ono ake amveketsa kulira.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mowabu waonongedwa; ang'ono ake amveketsa kulira.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mowabu waonongeka, ana ake akulira kwambiri.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mowabu wawonongeka; ana ake angʼonoangʼono akulira kwambiri.

Onani mutuwo



Yeremiya 48:4
6 Mawu Ofanana  

m'menemo mfumu inalola Ayuda okhala mu mzinda uliwonse asonkhane, ndi kulimbikira moyo wao, kuononga, kupha, ndi kupulula mphamvu yonse ya anthu ndi ya dziko yofuna kuwathira nkhondo, iwo, ana ao aang'ono, ndi akazi ao, ndi kulanda zofunkha zao,


Wodala iye amene adzagwira makanda ako, ndi kuwaphwanya pathanthwe.


Munthuyo akhale ngati mizinda imene Yehova anapasula, osalekerera; amve mfuu mamawa, ndi mkuwo pausana;


Mau amveka kuchokera ku Horonaimu, kufunkha ndi kuononga kwakukulu!


Pakuti adzakwera pa chikweza cha Luhiti ndi kulira kosaleka; pakuti pa chitsiko cha Horonaimu amva kulira kowawa kwa chionongeko.