Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yeremiya 41:4 - Buku Lopatulika

Ndipo panali atapita masiku awiri atamupha Gedaliya, anthu osadziwa,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo panali atapita masiku awiri atamupha Gedaliya, anthu osadziwa,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

M'maŵa mwake, anthu asanadziŵe kuti Gedaliya waphedwa,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mmawa mwake, anthu asanadziwe kuti Gedaliya waphedwa,

Onani mutuwo



Yeremiya 41:4
4 Mawu Ofanana  

Ismaele naphanso Ayuda onse okhala naye Gedaliya pa Mizipa, ndi Ababiloni amene anakomana nao komweko, amuna a nkhondo.


anadza anthu ochokera ku Sekemu, ndi ku Silo, ndi ku Samariya, anthu makumi asanu ndi atatu, atameta ndevu zao, atang'amba zovala zao, atadzitematema, anatenga nsembe zaufa ndi lubani m'manja mwao, kunka nazo kunyumba ya Yehova.


Ndipo Davide sadasunge wamoyo mwamuna kapena mkazi, kubwera nao ku Gati; popeza adati, Kuti angatiwulule, ndi kuti, Davide anatero, ndi makhalidwe ake ndi otere, masiku onse akukhala ku dziko la Afilisti.