Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yeremiya 24:4 - Buku Lopatulika

Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, kuti,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, kuti,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Chauta adandiwuza kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsono Yehova anandiwuza kuti,

Onani mutuwo



Yeremiya 24:4
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anati kwa ine, Kodi uona chiyani, Yeremiya? Ndipo ndinati, Nkhuyu, nkhuyu zabwino, nzabwino ndithu; zoipazo nzoipa ndithu, zosadyeka poti nzoipa.


Chifukwa Yehova, Mulungu wa Israele, atero, Monga nkhuyu zabwino izi, momwemo ndidzasamalira am'nsinga a Yuda, amene ndawachotsera m'malo muno kunka kudziko la Ababiloni, kuwachitira bwino.