Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yeremiya 2:1 - Buku Lopatulika

Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, nati,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, nati,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chauta adandiwuza kuti

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yehova anandiwuza kuti,

Onani mutuwo



Yeremiya 2:1
9 Mawu Ofanana  

Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, kuti, Yeremiya, uona chiyani? Ndipo ndinati, Ine ndiona nthyole ya katungurume.


Ndipo adzamenyana ndi iwe; koma sadzakuposa; chifukwa Ine ndili ndi iwe, ati Yehova, kukulanditsa.


Pita nufuule m'makutu a Yerusalemu, kuti, Yehova atero, Ndikumbukira za iwe kukoma mtima kwa ubwana wako, chikondi cha matomedwe ako; muja unanditsata m'chipululu m'dziko losabzalamo.


Mneneri wokhala ndi loto, anene loto lake; ndi iye amene ali ndi mau anga, anene mau anga mokhulupirika. Kodi phesi ndi chiyani polinganiza ndi tirigu? Ati Yehova.


Mau amene anadza kwa Yeremiya kuchokera kwa Yehova, kuti,


Ndipo mau a Yehova anandidzera, akuti,


Ndipo ndidzampatsa minda yake yampesa kuyambira pomwepo, ndi chigwa cha Akori chikhale khomo la chiyembekezo; ndipo adzavomereza pomwepo monga masiku a ubwana wake, ndi monga tsiku lokwera iye kutuluka m'dziko la Ejipito.


Kale Mulungu analankhula ndi makolo mwa aneneri m'manenedwe ambiri ndi mosiyanasiyana,


pakuti kale lonse chinenero sichinadze ndi chifuniro cha munthu; koma anthu a Mulungu, ogwidwa ndi Mzimu Woyera, analankhula.