Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yeremiya 18:3 - Buku Lopatulika

Ndipo ndinatsikira kunyumba ya woumba, ndipo, taonani, anaumba ntchito yake ndi njinga.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ndinatsikira kunyumba ya woumba, ndipo, taonani, anaumba ntchito yake ndi njinga.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Motero ndidatsikira ku nyumba ya woumba mbiya, ndipo ndidampeza akuumba mbiya pa mkombero.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Choncho ndinatsikira ku nyumba ya wowumba mbiya, ndipo ndinamuona akuwumba mbiya pa mkombero.

Onani mutuwo



Yeremiya 18:3
5 Mawu Ofanana  

Tauka, tatsikira kunyumba ya woumba, pamenepo ndidzakumvetsa mau anga.


Ndipo pamene mbiya alikuiumba ndi dothi inaonongeka m'dzanja la woumba, anaiumbanso mbiya ina, monga kunamkomera woumba kuiumba.


Koma Yona ananyamuka kuti athawire ku Tarisisi, kuzemba Yehova; ndipo anatsikira ku Yopa, napezako chombo chomuka ku Tarisisi, napereka ndalama zake, natsikira m'menemo, kuti apite nao ku Tarisisi kuzemba Yehova.


Muli abwenzi anga inu, ngati muzichita zimene ndikulamulani inu.


Potero, Mfumu Agripa, sindinakhale ine wosamvera masomphenya a Kumwamba;