Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yeremiya 18:2 - Buku Lopatulika

Tauka, tatsikira kunyumba ya woumba, pamenepo ndidzakumvetsa mau anga.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Tauka, tatsikira kunyumba ya woumba, pamenepo ndidzakumvetsa mau anga.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Nyamuka, upite ku nyumba ya munthu woumba mbiya, kumeneko ukamva mau anga.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Pita ku nyumba ya munthu wowumba mbiya, ndipo kumeneko ndikakuwuza mawu anga.”

Onani mutuwo



Yeremiya 18:2
10 Mawu Ofanana  

Nthawi imeneyo Yehova ananena ndi Yesaya, mwana wa Amozi, nati, Muka numasule chiguduli m'chuuno mwako, nuchichotse, nuvule nsapato yako kuphazi lako. Ndipo iye anatero, nayenda maliseche, ndi wopanda nsapato.


Atero Yehova kwa ine, Pita, udzigulire mpango wabafuta, nudzimangire m'chuuno mwako, usauike m'madzi.


Mau amene anadza kwa Yeremiya kuchokera kwa Yehova, kuti,


Ndipo ndinatsikira kunyumba ya woumba, ndipo, taonani, anaumba ntchito yake ndi njinga.


Koma akadaima mu upo wanga, akadamvetsa anthu anga mau anga, akadatembenuza iwo kunjira yao yoipa, ndi kuchoipa cha ntchito zao.


Anandionetsa chotere; ndipo taonani, Ambuye anaima pa khoma lomangidwa ndi chingwe cholungamitsira chilili; ndi chingwe cholungamitsira chilili m'dzanja lake.


komatu, uka, nulowe m'mzinda, ndipo kudzanenedwa kwa iwe chimene uyenera kuchita.


Kale Mulungu analankhula ndi makolo mwa aneneri m'manenedwe ambiri ndi mosiyanasiyana,