Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yeremiya 16:2 - Buku Lopatulika

Usatenge mkazi, usakhale ndi ana aamuna ndi aakazi m'malo muno.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Usatenge mkazi, usakhale ndi ana aamuna ndi aakazi m'malo muno.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Usadzakwatire, usadzabale ana aamuna kapena aakazi ku malo ano.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Usadzakwatire ndi kubereka ana aamuna kapena aakazi malo ano

Onani mutuwo



Yeremiya 16:2
9 Mawu Ofanana  

Ndipo anatuluka Loti nanena nao akamwini ake amene amayenera kukwatira ana ake aakazi, nati, Taukani, tulukani m'malo muno; popeza Yehova adzaononga mzindawu; koma akamwini ake anamyesa wongoseka.


Ndiponso mau a Yehova anadza kwa ine, kuti,


Pakuti Yehova atero za ana aamuna ndi za ana aakazi akubadwa m'malo muno, ndi za amai anawabala iwo, ndi za atate ao anawabala iwo m'dziko muno:


tengani akazi, balani ana aamuna ndi aakazi; kwatitsani ana anu aamuna, patsani ananu aakazi kwa amuna, kuti abale ana aamuna ndi aakazi; kuti mubalane pamenepo musachepe.


Mwaitana zondiopsa mozungulira ngati tsiku la msonkhano; panalibe wopulumuka ndi wotsala tsiku la mkwiyo wa Yehova; omwe ndinawaseweza ndi kuwalera, adaniwo anawatsiriza.


Koma tsoka ali nalo iwo akukhala ndi pakati, ndi akuyamwitsa ana m'masiku awo!


Koma tsoka iwo akukhala ndi pakati, ndi iwo akuyamwitsa ana masiku awo! Pakuti padzakhala chisauko chachikulu padziko, ndi mkwiyo pa anthu awa.


Chifukwa taonani masiku alinkudza, pamene adzati, Odala ali ouma ndi mimba yosabala, ndi mawere osayamwitsa.