Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yeremiya 13:8 - Buku Lopatulika

Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, kuti,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, kuti,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo mau a adandifikanso:

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamenepo Yehova anandiwuza kuti,

Onani mutuwo



Yeremiya 13:8
4 Mawu Ofanana  

Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine nthawi yachiwiri, kuti,


Ndipo ndinanka ku Yufurate, ndikukumba, nditenga mpango m'malo m'mene ndinaubisamo; ndipo, taonani, mpango unaonongeka, wosayenera kanthu.


Yehova atero, Momwemo ndidzaononga kudzitama kwa Yuda, ndi kudzitama kwakukulu kwa Yerusalemu.


Ndipo ndinapenya, ndipo taonani, kuthambo lokhala pamwamba pa mitu ya akerubi kudaoneka ngati mwala wasafiro, ngati maonekedwe a chifaniziro cha mpando wachifumu pamwamba pao.