Yeremiya 13:5 - Buku Lopatulika Ndipo ndinapita, ndinaubisa pa Yufurate, monga Yehova anandiuza ine. Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014 Ndipo ndinapita, ndinaubisa pa Yufurate, monga Yehova anandiuza ine. Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa Tsono ndidapitadi kukaubisa mpangowo ku Yufurate, monga momwe Chauta adaandiwuzira. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Ndipo ndinapitadi ndi kukabisa lambayo ku Yufurate, monga anenera Yehova. |
Ndipo panali atapita masiku ambiri, kuti Yehova anati kwa ine, Uka, pita ku Yufurate, nukatenge kumeneko mpango uja, ndinakuuza iwe ukaubise kumeneko.
M'mwemo ndinanenera monga anandiuza, ndipo ponenera ine panali phokoso; ndipo taonani, panali gobedegobede, ndi mafupa anasendererana, fupa kutsata fupa linzake.
Ndi chikhulupiriro Abrahamu, poitanidwa, anamvera kutuluka kunka kumalo amene adzalandira ngati cholowa; ndipo anatuluka wosadziwa kumene akamukako.