Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yeremiya 13:3 - Buku Lopatulika

Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine nthawi yachiwiri, kuti,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine nthawi yachiwiri, kuti,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chauta adandiwuzanso mau kachiŵiri kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka Yehova anandiyankhulanso kachiwiri kuti,

Onani mutuwo



Yeremiya 13:3
4 Mawu Ofanana  

Ndipo ndinagula mpango monga mwa mau a Yehova, ndi kuvala m'chuuno mwanga.


Tenga mpango umene unaugula, umene uli m'chuuno mwako, nuuke, nupite ku Yufurate, nuubise m'menemo m'phanga la m'mwala.


Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, kuti,


Yerusalemu, ndi mizinda ya Yuda, ndi mafumu ake omwe, ndi akulu ake, kuwayesa iwo bwinja, chizizwitso, chotsonyetsa, ndi chitemberero; monga lero lino;