Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yeremiya 11:2 - Buku Lopatulika

Imvani mau a pangano ili, nenani kwa anthu a Yuda, ndi anthu a Yerusalemu;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Imvani mau a pangano ili, nenani kwa anthu a Yuda, ndi anthu a Yerusalemu;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Imva mau a chipangano ichi, ndipo ulankhule nawo anthu a ku Yuda ndi a ku Yerusalemu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Imvani mawu a pangano ili, ndipo uwawuze anthu a ku Yuda ndi a ku Yerusalemu.

Onani mutuwo



Yeremiya 11:2
9 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehoyada anachita chipangano pakati pa Yehova ndi mfumu ndi anthu, akhale anthu a Yehova; pakati pa mfumunso ndi anthu.


Ndipo Yehoyada anachita pangano pakati pa iye, ndi anthu onse, ndi mfumu, kuti adzakhala anthu a Yehova.


Tsono mumtima mwanga nditi ndichite chipangano ndi Yehova Mulungu wa Israele, kuti mkwiyo wake waukali utembenuke kutichokera.


Ndipo mfumu inaimirira pokhala pake, ndi kuchita pangano pamaso pa Yehova, kuti adzayenda chotsata Yehova, ndi kusunga malamulo ake, ndi mboni zake, ndi malemba ake, ndi mtima wake wonse, ndi moyo wake wonse, kuchita mau a chipangano olembedwa m'bukumu.


Ndipo tsopano, ngati mudzamvera mau anga ndithu, ndi kusunga chipangano changa, ndidzakuyesani chuma changa cha padera koposa mitundu yonse ya anthu; pakuti dziko lonse lapansi ndi langa;


Mau amene anadza kwa Yeremiya kuchokera kwa Yehova, kuti,


Ndipo Yehova anati kwa ine, Lalikira mau onsewa m'mizinda ya Yuda, ndi m'miseu ya Yerusalemu, kuti, Tamvani mau a pangano ili, ndi kuwachita.