Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yeremiya 11:1 - Buku Lopatulika

Mau amene anadza kwa Yeremiya kuchokera kwa Yehova, kuti,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mau amene anadza kwa Yeremiya kuchokera kwa Yehova, kuti,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chauta adauza Yeremiya kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yehova anayankhula ndi Yeremiya kuti,

Onani mutuwo



Yeremiya 11:1
3 Mawu Ofanana  

Ndipo mau a Yehova anadza kwa iye, nati,


Tsanulirani ukali wanu pa amitundu osakudziwani Inu, ndi pa mabanja osaitana dzina lanu; pakuti anadya Yakobo, inde, anamudya namutha, napasula mokhalamo mwake.


Imvani mau a pangano ili, nenani kwa anthu a Yuda, ndi anthu a Yerusalemu;