Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yeremiya 1:4 - Buku Lopatulika

Ndipo anadza kwa ine mau a Yehova, kuti,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anadza kwa ine mau a Yehova, kuti,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chauta adandiwuza kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yehova anayankhula nane kuti,

Onani mutuwo



Yeremiya 1:4
5 Mawu Ofanana  

amene anamdzera mau a Yehova masiku a Yosiya mwana wake wa Amoni, mfumu ya Ayuda chaka chakhumi ndi chitatu cha ufumu wake.


Anamdzeranso masiku a Yehoyakimu mwana wake wa Yosiya, mfumu ya Yuda, kufikira Zedekiya mwana wake wa Yosiya mfumu ya Yuda atatsiriza zaka khumi ndi chimodzi; kufikira a ku Yerusalemu anatengedwa ndende mwezi wachisanu.


Ndisanakulenge iwe m'mimba ndinakudziwa, ndipo usanabadwe ndinakupatula iwe; ndinakuika kuti ukhale mneneri wa mitundu ya anthu.


anadzadi mau a Yehova kwa Ezekiele wansembe, mwana wa Buzi, m'dziko la Ababiloni kumtsinje Kebara; ndi pomwepo dzanja la Yehova lidamkhalira.


Ndipo kunali atatha masiku asanu ndi awiri, mau a Yehova anandidzera, ndi kuti,