Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yakobo 3:11 - Buku Lopatulika

Kodi kasupe atulutsira pa uno womwewo madzi okoma ndi owawa?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Kodi kasupe atulutsira pa uno womwewo madzi okoma ndi owawa?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kodi kasupe amatulutsa madzi omweka ndi oŵaŵa pa dzenje limodzimodzi?

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kodi madzi abwino ndi a mchere angatuluke pa kasupe mmodzi?

Onani mutuwo



Yakobo 3:11
3 Mawu Ofanana  

Monga kasupe atulutsa madzi ake, chomwecho atulutsa zoipa zake; chiwawa ndi kufunkha zimveka m'kati mwake; pamaso panga masiku onse pali kulira ndi mabala.


Mochokera m'kamwa momwemo mutuluka chiyamiko ndi temberero. Abale anga, izi siziyenera kutero.


Kodi mkuyu ukhoza kubala azitona, abale anga, kapena mpesa kubala nkhuyu? Kotero madzi amchere sangathe kutulutsa okoma.