Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yakobo 1:7 - Buku Lopatulika

Pakuti asayese munthu uyu kuti adzalandira kanthu kwa Ambuye;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti asayese munthu uyu kuti adzalandira kanthu kwa Ambuye;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Munthu wotere asamaganiza kuti nkudzalandira kanthu kwa Ambuye ai;

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Munthu wotere asayembekezere kulandira kalikonse kuchokera kwa Ambuye.

Onani mutuwo



Yakobo 1:7
7 Mawu Ofanana  

Nsembe ya oipa inyansa Yehova; koma pemphero la oongoka mtima limkondweretsa.


Nsembe ya oipa inyansa; makamaka pakudza nayo iwo mwachiwembu.


Ndipo pamene mutambasula manja anu, ndidzakubisirani inu maso anga; inde pochulukitsa mapemphero anu Ine sindidzamva; manja anu adzala mwazi.


Koma apemphe ndi chikhulupiriro, wosakayika konse; pakuti wokayikayo afanana ndi funde la nyanja lotengeka ndi mphepo ndi kuwinduka nayo.


munthu wa mitima iwiri akhala wosinkhasinkha panjira zake zonse.


Mupempha, ndipo simulandira, popeza mupempha koipa, kuti mukachimwaze pochita zikhumbitso zanu.