Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Tito 2:9 - Buku Lopatulika

Akapolo amvere ambuye ao a iwo okha, nawakondweretse m'zonse; osakana mau ao;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Akapolo amvere ambuye ao a iwo okha, nawakondweretse m'zonse; osakana mau ao;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Antchito azimvera ambuye ao, aziŵakondweretsa pa zonse. Asamatsutsana nawo

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Phunzitsa akapolo kuti azigonjera ambuye awo mu zinthu zonse ndi kuwakondweretsa. Asamatsutsane nawo

Onani mutuwo



Tito 2:9
5 Mawu Ofanana  

Komatu monga Mpingo amvera Khristu, koteronso akazi amvere amuna ao m'zinthu zonse.