Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Tito 2:4 - Buku Lopatulika

kuti akalangize akazi aang'ono akonde amuna ao, akonde ana ao,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

kuti akalangize akazi aang'ono akonde amuna ao, akonde ana ao,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

kuti choncho athe kuphunzitsa azimai achitsikana kukonda amuna ao ndi ana ao.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsono atha kulangiza amayi achichepere kukonda amuna awo ndi ana awo.

Onani mutuwo



Tito 2:4
5 Mawu Ofanana  

Koma amasiye aang'ono uwakane; pakuti pamene ayamba kumchitira Khristu chipongwe afuna kukwatiwa;


Chifukwa chake nditi akwatiwe amasiye aang'ono, nabale ana, naweruzire nyumba, osapatsa chifukwa kwa mdaniyo chakulalatira;


akazi aakulu ngati amai; akazi aang'ono ngati alongo, m'kuyera mtima konse.


Momwemonso akazi okalamba akhale nao makhalidwe oyenera anthu oyera, osadierekeza, osakodwa nacho chikondi cha pavinyo, akuphunzitsa zokoma;


akhale odziletsa, odekha, ochita m'nyumba mwao, okoma, akumvera amuna a iwo okha, kuti mau a Mulungu angachitidwe mwano.