Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Rute 2:5 - Buku Lopatulika

Nati Bowazi kwa mnyamata woyang'anira ochekawo, Mkazi uyu ngwa yani?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nati Bowazi kwa mnyamata woyang'anira ochekawo, Mkazi uyu ngwa yani?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Bowazi adafunsa kapitao wake amene ankayang'anira anthu okolola aja kuti, “Kodi mai uyu ndani?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Bowazi anafunsa kapitawo wake amene ankayangʼanira okolola aja kuti, “Mayi uyo ndi ndani?”

Onani mutuwo



Rute 2:5
4 Mawu Ofanana  

Ndipo taona, Bowazi anafuma ku Betelehemu, nati kwa ocheka, Yehova akhale nanu. Namyankha iwo, Yehova akudalitseni.


Ndipo mnyamata woyang'anira ochekawo anayankha nati, Ndiye mkazi Mmowabuyo anabwera ndi Naomi ku dziko la Mowabu;


ndi Salimoni anabala Bowazi, ndi Bowazi anabala Obedi;