Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 4:36 - Buku Lopatulika

ndipo owerengedwa ao monga mwa mabanja ao ndiwo zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi awiri kudza makumi asanu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo owerengedwa ao monga mwa mabanja ao ndiwo zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi awiri kudza makumi asanu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

ndipo chiŵerengero chao chidakwanira 2,750 potsata mabanja ao.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

atawawerenga mwa mafuko awo, anali 2,750.

Onani mutuwo



Numeri 4:36
2 Mawu Ofanana  

kuyambira a zaka makumi atatu ndi mphambu kufikira a zaka makumi asanu, onse akulowa utumikiwu, kuti agwire ntchito m'chihema chokomanako;


Awa ndi owerengedwa a mabanja a Akohati, onse akutumikira m'chihema chokomanako, amene Mose ndi Aroni anawawerenga monga mwa mau a Yehova mwa dzanja la Mose.