Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 34:26 - Buku Lopatulika

Wa fuko la ana a Isakara, kalonga Palatiele mwana wa Azani.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Wa fuko la ana a Isakara, kalonga Palatiele mwana wa Azani.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

M'fuko la ana a Isakara akhale Palatiele mwana wa Azani.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Palitieli mwana wa Azani, mtsogoleri wochokera ku fuko la Isakara,

Onani mutuwo



Numeri 34:26
3 Mawu Ofanana  

Pomwepo Isiboseti anatumiza namchotsera kwa mwamuna wake, kwa Palatiele mwana wa Laisi.


Wa fuko la ana a Zebuloni, kalonga Elizafani mwana wa Paranaki.


Wa fuko la ana a Asere, kalonga Ahihudi mwana wa Selomi.