Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 34:22 - Buku Lopatulika

Wa fuko la ana a Dani, kalonga Buki mwana wa Yogili.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Wa fuko la ana a Dani, kalonga Buki mwana wa Yogili.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

M'fuko la ana a Dani akhale Buki mwana wa Yogili.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Buki mwana wa Yogili, mtsogoleri wochokera ku fuko la Dani;

Onani mutuwo



Numeri 34:22
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anayandikiza, nati Tidzamangira zoweta zathu makola kuno, ndi ana athu mizinda;


Wa fuko la Benjamini, Elidadi mwana wa Kisiloni.


Wa ana a Yosefe; wa fuko la ana a Manase, kalonga Haniyele mwana wa Efodi.