Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 34:21 - Buku Lopatulika

Wa fuko la Benjamini, Elidadi mwana wa Kisiloni.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Wa fuko la Benjamini, Elidadi mwana wa Kisiloni.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

M'fuko la Benjamini akhale Elidadi mwana wa Kisiloni.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Elidadi mwana wa Kisiloni, wochokera ku fuko la Benjamini;

Onani mutuwo



Numeri 34:21
4 Mawu Ofanana  

Benjamini ndiye mmbulu wakulusalusa; m'mamawa adzadya chomotola, madzulo adzagawa zofunkha.


Apo pali Benjamini wamng'ono, wakuwachita ufumu, akulu a Yuda, ndi a upo wao, akulu a Zebuloni, akulu a Nafutali.


Wa fuko la ana a Dani, kalonga Buki mwana wa Yogili.


Za Benjamini anati, Wokondedwa wa Yehova adzakhala ndi Iye mokhazikika; am'phimba tsiku lonse, inde akhalitsa pakati pa mapewa ake.