Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 34:20 - Buku Lopatulika

Wa fuko la ana a Simeoni, Semuele mwana wa Amihudi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Wa fuko la ana a Simeoni, Semuele mwana wa Amihudi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

M'fuko la ana a Simeoni akhale Semuele mwana wa Amihudi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Semueli mwana wa Amihudi, wochokera ku fuko la Simeoni;

Onani mutuwo



Numeri 34:20
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anatenganso pakati, nabala mwana wamwamuna nati, Chifukwa anamva Yehova kuti anandida ine, anandipatsa ine mwana wamwamuna uyunso; ndipo anamutcha dzina lake Simeoni.


Simeoni ndi Levi ndiwo abale; zida za mphulupulu ndizo malupanga ao.


Ndi kumalire a Benjamini, kuyambira mbali ya kum'mawa kufikira mbali ya kumadzulo; Simeoni, gawo limodzi.