Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 33:44 - Buku Lopatulika

Nachokera ku Oboti, nayenda namanga mu Iyeabarimu, m'malire a Mowabu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nachokera ku Oboti, nayenda namanga m'Iyeabarimu, m'malire a Mowabu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adanyamuka ku Oboti, nakamanga mahema ao ku Iyeabarimu, m'dziko la Mowabu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atachoka ku Oboti anakamanga ku Iye-Abarimu.

Onani mutuwo



Numeri 33:44
4 Mawu Ofanana  

Pamenepo ana a Israele anayenda ulendo, namanga mahema mu Oboti.


Ndipo anachoka ku Oboti, namanga mahema ku Iyeabarimu, m'chipululu chakuno cha Mowabu, kotulukira dzuwa.


Nachokera ku Punoni, nayenda namanga mu Oboti.


Nachokera ku Iyimu, nayenda namanga mu Diboni Gadi.