Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 33:40 - Buku Lopatulika

Ndipo Mkanani, mfumu ya Aradi, wakukhala kumwera m'dziko la Kanani, anamva za kudza kwao kwa ana a Israele.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Mkanani, mfumu ya Aradi, wakukhala kumwera m'dziko la Kanani, anamva za kudza kwao kwa ana a Israele.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mfumu ya ku Aradi, Mkanani amene ankakhala m'dziko la Kanani, adamva kuti Aisraele akubwera.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mfumu ya Akanaani ya ku Aradi yomwe inkakhala ku Negevi kummwera kwa Kanaani, inamva kuti Aisraeli akubwera.

Onani mutuwo



Numeri 33:40
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Abramu anayenda ulendo wake, nayendayenda kunka kumwera.


Ndipo Aroni ndiye wa zaka zana limodzi mphambu makumi awiri kudza zitatu pakufa iye m'phiri la Hori.


Ndipo anachokera kuphiri la Hori, nayenda namanga mu Zalimona.