Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 33:39 - Buku Lopatulika

Ndipo Aroni ndiye wa zaka zana limodzi mphambu makumi awiri kudza zitatu pakufa iye m'phiri la Hori.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Aroni ndiye wa zaka zana limodzi mphambu makumi awiri kudza zitatu pakufa iye m'phiri la Hori.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Aroniyo anali wa zaka 123 za kubadwa, pamene adamwalira pa phiri la Hori.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Aaroni anamwalira pa phiri la Hori ali ndi zaka 123.

Onani mutuwo



Numeri 33:39
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Mose anali nazo zaka makumi asanu ndi atatu, ndi Aroni anali nazo zaka makumi asanu ndi atatu kudza zitatu, pamene ananena ndi Farao.


Ndipo Aroni wansembe anakwera m'phiri la Hori pa mau a Yehova, nafa komweko, atatuluka ana a Israele m'dziko la Ejipito zaka makumi anai, mwezi wachisanu, tsiku loyamba la mwezi.


Ndipo Mkanani, mfumu ya Aradi, wakukhala kumwera m'dziko la Kanani, anamva za kudza kwao kwa ana a Israele.