Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 33:34 - Buku Lopatulika

Nachokera ku Yotibata, nayenda namanga mu Aborona.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nachokera ku Yotibata, nayenda namanga m'Aborona.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adanyamuka ku Yotibata, nakamanga mahema ao ku Aborona.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atachoka ku Yotibata anakamanga ku Abirona.

Onani mutuwo



Numeri 33:34
3 Mawu Ofanana  

Nachokera ku Hori Hagidigadi, nayenda namanga mu Yotibata.


Nachokera ku Aborona, nayenda namanga mu Eziyoni-Gebere.


Kuchokerako ananka ulendo ku Gudigoda, ndi kuchokera ku Gudigoda kunka ku Yotibata, dziko la mitsinje yamadzi.