Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 33:30 - Buku Lopatulika

Nachokera ku Hasimona, nayenda namanga mu Meseroti.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nachokera ku Hasimona, nayenda namanga m'Meseroti.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adanyamuka ku Hasimona, nakamanga mahema ao ku Meseroti.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atachoka ku Hasimona anakamanga ku Moseroti.

Onani mutuwo



Numeri 33:30
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Mose anavula Aroni zovala zake, naveka Eleazara mwana wake; ndipo Aroni anafa pomwepo pamwamba paphiri. Pamenepo Mose ndi Eleazara anatsika m'phirimo.


Nachokera ku Mitika, nayenda namanga mu Hasimona.


Nachokera ku Meseroti, nayenda namanga mu Bene-Yaakani.


nufe m'phiri m'mene ukweramo, nuitanidwe kunka kwa anthu a mtundu wako; monga Aroni mbale wako anafa m'phiri la Hori, naitanidwa kunka kwa anthu a mtundu wake;