Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 33:26 - Buku Lopatulika

Nachokera ku Makeloti, nayenda namanga mu Tahata.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nachokera ku Makeloti, nayenda namanga m'Tahata.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adanyamuka ku Makeloti, nakamanga mahema ao ku Tahati.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atachoka ku Mekheloti anakamanga ku Tahati.

Onani mutuwo



Numeri 33:26
2 Mawu Ofanana  

Nachokera ku Harada, nayenda namanga mu Makeloti.


Nachokera ku Tahata, nayenda namanga mu Tera.