Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 33:21 - Buku Lopatulika

Nachokera ku Libina, nayenda namanga mu Risa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nachokera ku Libina, nayenda namanga m'Risa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adanyamuka ku Libina, nakamanga mahema ao ku Risa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atachoka ku Libina anakamanga ku Risa.

Onani mutuwo



Numeri 33:21
3 Mawu Ofanana  

Nachokera ku Rimoni-Perezi, nayenda namanga mu Libina.


Nachokera Risa, nayenda namanga mu Kehelata.


Awa ndi mau amene Mose ananena kwa Israele wonse, tsidya la Yordani m'chipululu, m'chidikha cha pandunji pa Sufu, pakati pa Parani, ndi Tofele, ndi Labani, ndi Hazeroti, ndi Dizahabu.