Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 33:20 - Buku Lopatulika

Nachokera ku Rimoni-Perezi, nayenda namanga mu Libina.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nachokera ku Rimoni-Perezi, nayenda namanga m'Libina.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adanyamuka ku Rimoni-Perezi, nakamanga mahema ao ku Libina.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atachoka ku Rimoni-Perezi anakamanga ku Libina.

Onani mutuwo



Numeri 33:20
6 Mawu Ofanana  

Ndipo kazembeyo anabwerera, napeza mfumu ya Asiriya ilikuponyana nkhondo ndi Libina; pakuti anamva kuti inachoka ku Lakisi.


Ndipo Mose anawatuma a fuko limodzi chikwi chimodzi, kunkhondo, iwowa ndi Finehasi mwana wa Eleazara wansembe, kunkhondo, ndi zipangizo zopatulika, ndi malipenga oliza m'dzanja lake.


Nachokera ku Ritima, nayenda namanga mu Rimoni-Perezi.


Nachokera ku Libina, nayenda namanga mu Risa.


Awa ndi mau amene Mose ananena kwa Israele wonse, tsidya la Yordani m'chipululu, m'chidikha cha pandunji pa Sufu, pakati pa Parani, ndi Tofele, ndi Labani, ndi Hazeroti, ndi Dizahabu.


Pamenepo Yoswa ndi Aisraele onse naye anapitirira kuchokera ku Makeda kunka ku Libina, nathira nkhondo pa Libina;